Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 10/14 tsamba 2
  • Ndandanda ya Mlungu wa October 20

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa October 20
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 20
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 10/14 tsamba 2

Ndandanda ya Mlungu wa October 20

MLUNGU WOYAMBIRA OCTOBER 20

Nyimbo Na. 15 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 3 ndime 1-10 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Deuteronomo 7-10 (Mph. 10)

Na. 1: Deuteronomo 9:15-29 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Chifukwa Chake Zinali Zotheka Kuti Munthu Wangwiro Achimwe—rs tsa. 358 ndime 1-4 (Mph. 5)

Na. 3: Tisamakayikire Zimene Yehova Wasankha—Aroma 11:33; 1 Yoh. 4:8 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Nyimbo Na. 116

Mph. 15: “Mmene Tingafotokozere Zimene Timakhulupirira Zokhudza Chaka cha 1914.” Nkhani yokambirana. Funsani omvera kuti ayankhe mafunso omwe ali ndi timadonthowo.

Mph. 15: Nkhani Zomwe Zingatithandize Kufotokoza Zomwe Timakhulupirira Zokhudza 1914. Yambani ndi kuchita chitsanzo cha mphindi 7 pogwiritsa ntchito tchati chomwe chili mu Nsanja ya Olonda ya November 1, 2014, patsamba 11. Chitsanzocho chisonyeze wofalitsa akufotokozera munthu amene amaphunzira naye Baibulo mmene ulosi wopezeka pa Danieli chaputala 4 ukugwirizanirana ndi Ufumu wa Mulungu. Pemphani omvera kuti afotokoze zomwe wofalitsayo anachita zimene zathandiza wophunzira Baibuloyo. Pomaliza werengani Chivumbulutso 12:10, 12 ndipo pemphani omvera kuti afotokoze chifukwa chake kudziwa kuti Ufumu wa Mulungu unayamba kulamulira mu 1914 kumatithandiza kuti tizilalikira modzipereka.

Nyimbo Na. 133 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena