Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 12/14 tsamba 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa December 22

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa December 22
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 22
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 12/14 tsamba 3

Ndandanda ya Mlungu wa December 22

MLUNGU WOYAMBIRA DECEMBER 22

Nyimbo Na. 132 ndi Pemphero

Phunziro la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 6 ndime 1-8 (Mph. 30)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: Yoswa 9-11 (Mph. 10)

Na. 1: Yoswa 9:16-27 (Osapitirira mph. 4)

Na. 2: Palibe Mbali ya Munthu Imene Imakhalabe ndi Moyo Munthu Akafa—rs tsa. 321 ndime 6–tsa. 322 ndime 3 (Mph. 5)

Na. 3: Chifukwa Chake Tiyenera Kukhala pa Ubwenzi Wabwino ndi Yehova Ndiponso Anthu Amene Amamukonda—lv tsa. 26-27 ndime 4-7 ndi bokosi patsamba 29 (Mph. 5)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezi Uno: Tizipereka zinthu “zabwino” zochokera m’chuma chomwe tinapatsidwa.—Mat. 12:35a.

Nyimbo Na. 119

Mph. 5: Zofunika pampingo.

Mph. 25: “Sukulu ya Utumiki wa Mulungu ya 2015 Itithandiza Kuti Tiziphunzitsa Mwaluso.” Nkhani yokambirana yokambidwa ndi woyang’anira sukulu. Woyang’anira sukulu angasankhe kuti ndime zina ziwerengedwe musanazikambirane. Fotokozani chimene chasintha pa nkhani Na. 1, nthawi ya mfundo zazikulu za Baibulo komanso malangizo omwe woyang’anira sukulu azipereka. Werengani ndime 7 ndipo mukamaliza kuikambirana chitani chitsanzo chosonyeza mkulu akuchita kulambira kwa pabanja ndi mkazi komanso mwana wake pogwiritsa ntchito nkhani yomwe ili patsamba 14 m’kabuku kakuti, Kodi M’Baibulo Muli Nkhani Zotani? Limbikitsani onse kuti ayesetse kupindula mokwanira ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu. Alimbikitseninso kuti azigwiritsa ntchito bwino buku la Pindulani ndi Sukulu ya Utumiki wa Mulungu.

Nyimbo Na. 117 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena