Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/15 tsamba 1
  • Ndandanda ya Mlungu wa November 9

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ndandanda ya Mlungu wa November 9
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Timitu
  • MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 9
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 11/15 tsamba 1

Ndandanda ya Mlungu wa November 9

MLUNGU WOYAMBIRA NOVEMBER 9

Nyimbo Na. 44 ndi Pemphero

cl mutu 21 ndime 9-15 (30 min.)

Sukulu ya Utumiki wa Mulungu:

Kuwerenga Baibulo: 1 Mbiri 21-25 (8 min.)

Na. 1: 1 Mbiri 23:1-11 (Osapitirira 3 min.)

Na. 2: Kodi Munthu Ali ndi Mzimu Umene Suufa?—bh tsa. 209-211 (5 min.)

Na. 3: Kodi Aramagedo N’chiyani?—rs tsa. 37-38 ndime 5 (5 min.)

Msonkhano wa Utumiki:

Mutu wa Mwezu Uno: “Ineyo ndinabzala, Apolo anathirira, koma Mulungu ndiye anakulitsa.”—1 Akor. 3:6.

Nyimbo Na. 98

10 min: “Ineyo Ndinabzala, Apolo Anathirira, Koma Mulungu Ndiye Anakulitsa.” Nkhani yochokera pa mutu wa mwezi uno. (1 Akor. 3:6) Ngati nthawi ilipo, fotokozani mfundo za mu Nsanja ya Olonda ya March 1, 1993, tsamba 20 mpaka 23. Fotokozani mwachidule nkhani zimene tiphunzire pa Msonkhano wa Utumiki mwezi wa November ndiponso kugwirizana kwake ndi mutu wa mweziwu.

20 min: “Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Kugawira Buku Lakuti Baibulo Limaphunzitsa Chiyani.” Nkhani yokambirana. Chitani zitsanzo ziwiri. Chitsanzo chimodzi chisonyeze zimene zafotokozedwa mu nkhaniyi, china chisonyeze njira imene mukuona kuti imathandiza kwambiri.

Nyimbo Na. 111 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena