Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 March tsamba 7
  • Aisiraeli Anaiwala Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Aisiraeli Anaiwala Yehova
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Yofanana
  • Samalani, Mtima Ndi Wonyenga
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • Yeremiya—Mneneri Wachilendo wa Ziweruzo za Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1988
  • “Ndaika Mawu Anga M’kamwa Mwako”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
  • “Sindingathe Kukhala Chete”
    Zimene Mulungu Akutiuza Kudzera mwa Yeremiya
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 March tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | YEREMIYA 12-16

Aisiraeli Anaiwala Yehova

Yeremiya anapatsidwa ntchito yovuta kwambiri imene inasonyeza zimene Yehova ankafuna kuchita powononga Aisiraeli osamva a ku Yuda ndiponso ku Yerusalemu.

Yeremiya anayenda kuchokera ku Yerusalemu kupita kumtsinje wa Firate n’kubwereranso

Yeremiya anagula lamba wansalu

13:1, 2

  • Anamanga lambayo m’chiuno ndipo zinkaimira ubwenzi wolimba umene Aisiraeli akanakhala nawo ndi Yehova

Yeremiya anatenga lambayo n’kupita naye kumtsinje wa Firate

13:3-5

  • Iye anamubisa mumng’alu wa m’phanga n’kubwerera ku Yerusalemu

Yeremiya anabwereranso kumtsinje wa Firate kukatenga lambayo

13:6, 7

  • Anali atawonongeka

Yehova anafotokoza tanthauzo la zimenezi pambuyo poti Yeremiya wamaliza ntchitoyi

13:8-11

  • Ntchitoyi inkaoneka ngati yopanda pake, komabe Yeremiya anamvera ndi mtima wonse ndipo izi zinathandiza kuti Yehova afike anthuwo pamtima

KODI MUKUDZIWA?

Mtunda wochokera ku Yerusalemu kupita kumtsinje wa Firate unali wa makilomita pafupifupi 500. Kuti Yeremiya ayende maulendo onse awiriwa, anayenera kuyenda mtunda wa makilomita pafupifupi 2,000, zomwe mwina zinamutengera miyezi ingapo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena