Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 May tsamba 6
  • May 22-28

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 22-28
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 May tsamba 6

May 22-28

YEREMIYA 44-48

  • Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Leka ‘Kufunafuna Zinthu Zazikulu’”: (10 min.)

    • Yer. 45:2,3​—Baruki sankasangalala chifukwa cha maganizo olakwika amene anali nawo (jr 104-105 ¶4-6)

    • Yer. 45:4,5a​—Yehova anathandiza Baruki mokoma mtima (jr 103 ¶2)

    • Yer. 45:5b​—Baruki anapulumutsa moyo wake chifukwa choika maganizo ake pa zinthu zofunika kwambiri (w16.07 8 ¶6)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Yer. 48:13​—N’chifukwa chiyani ‘Amowabu anachita manyazi ndi Kemosi’? (it-1-E 430)

    • Yer. 48:42​—Kodi kuganizira za chiweruzo chimene Yehova anapereka kwa Amowabu kungalimbitse bwanji chikhulupiriro chathu? (it-2-E 422 ¶2)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Yer. 47:1-7

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) hf​—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) hf​—Muuzeni nkhani imene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) lv 199 ¶9-10​—Mwachidule sonyezani wophunzira mmene angafufuzire malangizo pa nkhani yokhudza vuto linalake limene akukumana nalo.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 150

  • Achinyamata​—Musamafunefune Zinthu Zazikulu: (15 min.) Onetsani ndiponso kukambirana vidiyo yakuti Zimene Achinyamata Amafunsa​—Kodi Ndidzachita Zotani Pamoyo Wanga?​—Zimene Anasankha.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 1 ¶1-10 komanso Kalata Yochokera ku Bungwe Lolamulira

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 17 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena