Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsamba 5
  • June 19-25

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • June 19-25
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 June tsamba 5

June 19-25

EZEKIELI 1-5

  • Nyimbo Na. 75 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Ezekieli Ankasangalala Kulengeza Uthenga wa Mulungu”: (10 min.)

    • [Onetsani vidiyo yakuti, Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Ezekieli.]

    • Ezek. 2:9–3:2​—Ezekieli anadya mpukutu wokhala ndi “nyimbo zoimba polira, mawu odandaula ndi mawu olira” (w08 7/15 8 ¶6-7; it-1-E 1214)

    • Ezek. 3:3​—Ezekieli ankasangalala kutumikira Yehova monga mneneri (w07 7/1 12 ¶3)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Ezek. 1:20, 21, 26-28​—Kodi galeta lakumwamba limaimira chiyani? (w07 7/1 11 ¶6)

    • Ezek. 4:1-7​—Kodi Ezekieli anachitadi zinthu zofanizira kuzingidwa kwa Yerusalemu? (w07 7/1 12 ¶4)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Ezek. 1:1-14

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) T-32​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) T-32​—Muonetseni Vidiyo Yothandiza Pogawira Kabuku Kakuti Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala, kenako mugawireni kabukuko.

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 6 min.) bh 143 ¶20-21​—Sonyezani mmene tingafikire pamtima wophunzira wathu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 153

  • “Muzisangalala Mukamalalikira Uthenga Wabwino”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onetsani vidiyo yakuti Kusinkhasinkha Kungatithandize Kukhala Wosangalala (imapezeka pamene palembedwa kuti BAIBULO).

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu  2 ¶23-34

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 32 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena