Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 September tsamba 5
  • September 18-24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 18-24
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 September tsamba 5

September 18-24

Danieli 1-3

  • Nyimbo Na. 131 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kukhala Okhulupirika kwa Yehova Kumabweretsa Madalitso”: (10 min.)

    • [Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Danieli.]

    • Dan. 3:16-20​—Anzake a Danieli analimba mtima n’kukana kuchita zinthu zimene zikanawapangitsa kuti akhale osakhulupirika kwa Yehova (w15 7/15 25 ¶15-16)

    • Dan. 3:26-29​—Kukhulupirika kwawo kunachititsa kuti Yehova atamandidwe ndipo anawadalitsa (w13 1/15 10 ¶13)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Dan. 1:5, 8​—N’chifukwa chiyani Danieli ndi anzake atatu aja ankaona kuti adetsedwa akadya zakudya zabwino zochokera kwa mfumu? (it-2 382)

    • Dan. 2:44​—N’chifukwa chiyani Ufumu wa Mulungu udzaphwanye maufumu a padziko lapansi omwe ndi mbali zosiyanasiyana za chifaniziro chomwe Nebukadinezara analota? (w12 6/15 17, bokosi; w01 10/15 6 ¶4)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Dan. 2:31-43

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Yes. 40:22​—Kuphunzitsa Choonadi​—Muuzeni zimene mudzakambirane ulendo wotsatira.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Aroma 15:4​—Kuphunzitsa Choonadi​—Musiyireni khadi lodziwitsa anthu za JW.ORG.

  • Nkhani: (Osapitirira 6 min.) w17.02 29-30​—Mutu: Kodi Yehova Amayamba Waganizira Kaye Zimene Tingapirire Ndiyeno N’kusankha Mayesero Oti Tikumane Nawo?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 63

  • “Muzikhala Okhulupirika Mukakumana ndi Mayesero”: (8 min.) Nkhani yokambirana.

  • “Muzikhala Okhulupirika Wachibale Wanu Akachotsedwa”: (7 min.) Nkhani yokambirana.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 7 ¶1-9

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 101 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena