Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 101
  • Tilalikire Choonadi cha Ufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tilalikire Choonadi cha Ufumu
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kudziŵitsa Chowonadi Chaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 101

Nyimbo 101

Tilalikire Choonadi cha Ufumu

Losindikizidwa

(Machitidwe 20:20, 21)

1. Poyamba sitinkadziwa

Zinthu zoti tizichita.

Yehova ’natumiza

Choonadi ndi kuwala.

Ndipo tinazindikira

Chifuniro cha Yehova

Kuti tim’tumikire

Ndi kumalengeza dzina lake.

Timalalikira ndithu

Pamakomo ndi mumsewu

Timathandiza anzathu

Choonadi adziwetu.

Tiyenitu tiyesetse

Mulungu titumikire

Kufikira Yehova

Atanena kuti tamaliza.

(Onaninso Yos. 9:9; Yes. 24:15; Yoh. 8:12, 32.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena