Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 December tsamba 6
  • December 25-31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • December 25-31
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 December tsamba 6

December 25-31

MALAKI 1-4

  • Nyimbo Na. 36 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Ukwati Wanu Umakondweretsa Yehova?”: (10 min.)

    • [Onetsani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Malaki.]

    • Mal. 2:13, 14​—Yehova amadana ndi khalidwe lachinyengo m’banja (jd 125-126 ¶4-5)

    • Mal. 2:15, 16​—Muzikhala wokhulupirika kwa mwamuna kapena mkazi wanu (w02 5/1 18 ¶19)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mal. 1:10​—N’chifukwa chiyani tiyenera kuchita zinthu zokhudza kulambira chifukwa chokonda Mulungu komanso anzathu? (w07 12/15 27 ¶1)

    • Mal. 3:1​—Kodi vesili linakwaniritsidwa bwanji m’nthawi ya atumwi komanso m’nthawi yathu ino? (w13 7/15 10-11 ¶5-6)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mal. 1:1-10

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) 1 Akor. 15:26​—Kuphunzitsa Choonadi.

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yes. 26:19; 2 Akor. 1:3, 4​—Kuphunzitsa Choonadi. (Onani mwb16.08 8 ¶2.)

  • Nkhani: (Osapitirira 6 min.) w07 12/15 28 ¶1​—Mutu: Kodi Masiku Ano Timapereka Bwanji kwa Yehova Gawo Limodzi mwa Magawo 10 Alionse a Zinthu Zathu?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 87

  • “Chikondi Chenicheni”: (15 min.) Mafunso ndi mayankho.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) kr mutu 12 ¶1-8 komanso tsamba 121

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 114 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena