Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 November tsamba 3
  • November 12-18

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • November 12-18
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Timitu
  • MOYO WATHU WACHIKHRISTU
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 November tsamba 3

November 12-18

MACHITIDWE 1-3

  • Nyimbo Na. 104 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mpingo Wachikhristu Unalandira Mzimu Woyera”: (10 min.)

    • [Onerani vidiyo yakuti Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Machitidwe.]

    • Mac. 2:1-8, 14, 37, 38, 41​—Atalandira mzimu woyera, ophunzira a Yesu anayamba kulalikira ndipo izi zinachititsa kuti anthu pafupifupi 3,000 abatizidwe

    • Mac. 2:42-47​—Ophunzira a Yesu anasonyeza mtima wowolowa manja komanso wochereza ndipo izi zinathandiza kuti anthu amene anangobatizidwa kumene akhalebe kwa kanthawi ku Yerusalemu kuti alimbitse chikhulupiriro chawo (w86 12/1 29 ¶4-5, 7)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Mac. 3:15​—N’chifukwa chiyani Yesu amatchedwa “Mtumiki Wamkulu wa moyo”? (it-2 61 ¶1)

    • Mac. 3:19​—Kodi vesili likusonyeza bwanji mmene Yehova amachitira akamakhululukira munthu amene walapa? (cl 265 ¶14)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Mac. 2:1-21

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsirani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba.

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Nkhani: (Osapitirira 6 min.) it-1 129 ¶2-3​—Mutu: N’chifukwa Chiyani Panasankhidwa Mtumwi Wolowa M’malo Mwa Yudasi Pamene Atumwi Ena Okhulupirika Akamwalira Sankalowedwa M’malo ndi Ena?

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 85

  • “Tizichita Zinthu Mogwirizana Tikamalalikira M’gawo la Zinenero Zambiri”: (15 min.) Nkhani yokambirana yokambidwa ndi woyang’anira utumiki. Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi. Fotokozani dongosolo lomwe mpingo wanu wakonza lokhudza kulalikira m’gawo la zinenero zambiri.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 13

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 97 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena