Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 May tsamba 5
  • Mukhoza Kumasangalalabe Ngakhale Muli ndi “Munga M’thupi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mukhoza Kumasangalalabe Ngakhale Muli ndi “Munga M’thupi”
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Paulo Anali ndi “Munga M’thupi”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Kutumikira Yehova Monga Banja Logwirizana
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kulimbana ndi “Munga M’thupi”
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Anthu Okhulupirika Analimbana ndi Minga M’matupi Awo
    Nsanja ya Olonda—2002
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 May tsamba 5
Talita akuonera vidiyo limodzi ndi mayi ake komanso mchemwali wake ndipo mayi ake akufotokozera zimene zikuchitika m’vidiyoyo

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Mukhoza Kumasangalalabe Ngakhale Muli ndi “Munga M’thupi”

M’masiku otsiriza ano atumiki onse a Mulungu akukumana ndi mavuto aakulu okhala ngati munga. (2 Tim. 3:1) Kodi tingasonyeze bwanji kuti timadalira Yehova kuti atithandize kupilira mavutowa? Onerani vidiyo yakuti “Maso a Anthu Akhungu Adzatsegulidwa” kuti mudziwe zimene Talita Alnashi ndi makolo ake anachita. Mukaonera vidiyoyi yankhani mafunso awa:

  • Kodi Talita akulimbana ndi vuto lanji?

  • Ndi malonjezo ati a m’Baibulo omwe athandiza Talita ndi makolo ake kuti asamakhale ndi nkhawa kwambiri?

  • Kodi Makolo a Talita anasonyeza bwanji kuti amadalira Yehova mwana wawo atangochitidwa kumene opaleshoni?

  • Kodi makolo a Talita amagwiritsa ntchito bwanji zinthu zomwe gulu lathu limatipatsa pothandiza mwana wawo kuti azikonda kwambiri Mulungu?

  • N’chiyani chikusonyeza kuti Talita akukula mwauzimu ngakhale kuti ali ndi “munga m’thupi”?

  • Kodi nkhani ya Talita yakulimbikitsani bwanji?

Talita akufotokoza zimene akuyembekezera, akuwerenga pogwiritsa ntchito kompyuta, akuyankha pamisonkhano, ali mu utumiki ndi bambo ake
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena