Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 4
  • September 16-22

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • September 16-22
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 4

September 16-22

AHEBERI 11

  • Nyimbo Na. 119 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 3 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chikhulupiriro ndi Chofunika Kwambiri”: (10 min.)

    • Aheb. 11:1​—Kodi chikhulupiriro chimatanthauza chiyani? (w16.10 27 ¶6)

    • Aheb. 11:6​—Chikhulupiriro n’chofunika kuti tizikondweretsa Mulungu (w13 11/1 11 ¶2-5)

    • Aheb. 11:33-38​—Chikhulupiriro chinathandiza atumiki akale a Mulungu kupirira mayesero omwe ankakumana nawo (w16.10 23 ¶10-11)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (8 min.)

    • Aheb. 11:4​—Kodi n’chiyani chinathandiza Abele kukhala ndi chikhulupiriro cholimba? (it-1 804 ¶5)

    • Aheb. 11:5​—Kodi Inoki anadalitsidwa bwanji chifukwa cha chikhulupiriro chake? (wp17.1 12-13)

    • Kodi mwaphunzira zotani zokhudza Yehova pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

    • Kodi ndi mfundo zina ziti zothandiza zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Aheb. 11:1-16 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Onerani ndi kukambirana mfundo za m’vidiyoyi.

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 3)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. M’patseni kapepala komuitanira kumisonkhano yathu, kenako yerekezerani kumuonetsa vidiyo yakuti Kodi pa Nyumba ya Ufumu Pamachitika Zotani? (th phunziro 11)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 3

  • “Kodi Mudzatani pa Nthawi ya Chilala?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 51

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 122 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena