Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 September tsamba 4
  • Chikhulupiriro ndi Chofunika Kwambiri

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chikhulupiriro ndi Chofunika Kwambiri
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Muzikhala ndi Makhalidwe Amene Mulungu Amasangalala Nawo​—Chikhulupiriro
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Nkhani Zimene Zili M’magaziniyi
    Galamukani!—2022
  • Muzitsanzira Yesu pa Nkhani Yochitira Ena Chifundo
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • “Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 September tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AHEBERI 11

Chikhulupiriro ndi Chofunika Kwambiri

11:1, 6, 33-38

Kodi chikhulupiriro cholimba chingakuthandizeni bwanji pa zochitika zotsatirazi?

  • Woyang’anira dera ku Africa akulemba lipoti lake

    Ngati mutapatsidwa utumiki wovuta kwambiri.​—Aheb. 11:8-10

  • Banja limene laferedwa lazungulira bokosi la maliro limene laikidwa maluwa

    Ngati munthu amene mumamukonda wamwalira.​—Aheb. 11:17-19

  • Pa nthawi ya chisautso chachikulu, mabanja angapo ali m’chipinda chapansi ndipo akuphunzira Baibulo pamodzi

    Ngati akuluakulu a boma ataletsa kulambira kwathu.​—Aheb. 11:23-26

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena