Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsamba 6
  • February 17-23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • February 17-23
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 February tsamba 6

February 17-23

GENESIS 18-19

  • Nyimbo Na. 1 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (Osapitirira 1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “‘Woweruza wa Dziko Lonse Lapansi’ Anawononga Sodomu ndi Gomora”: (10 min.)

    • Gen. 18:23-25​—Abulahamu ankakhulupirira kuti Yehova amapereka chiweruzo cholungama nthawi zonse (w17.04 18 ¶1)

    • Gen. 18:32​—Yehova anatsimikiza kuti sawononga Sodomu ngati mutapezeka anthu 10 olungama (w18.08 30 ¶4)

    • Gen. 19:24, 25​—Yehova anawononga Sodomu ndi Gomora chifukwa anthu ake anali oipa (w10 11/15 26 ¶12)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Ge 18:1, 22​—Kodi Yehova “anaonekera kwa Abulahamu” komanso “anatsala ataima” nayebe m’njira yotani? (w88 5/15 23 ¶4-5)

    • Gen. 19:26​—N’chifukwa chiyani mkazi wa Loti anasanduka “chipilala chamchere”? (w19.06 20 ¶3)

    • Kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 18:1-19 (th phunziro 12)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi n’chiyani chakusangalatsani ndi zimene wofalitsayu ananena asanawerenge lemba? Kodi anathandiza bwanji womvetsera wake kuona mmene angagwiritsire ntchito mfundo ya lembalo?

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 6)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. Kenako m’patseni buku lakuti Zimene Baibulo Limaphunzitsa, ndipo kambiranani chithunzi chomwe chili patsamba 98. (th phunziro 9)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 35

  • “Kodi Mumapindula ndi Kabuku ka Kuphunzira Malemba Tsiku ndi Tsiku?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti, Musamakonde Dziko (1 Yoh. 2:15).

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 73

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 102 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena