Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 February tsamba 6
  • “Woweruza wa Dziko Lonse Lapansi” Anawononga Sodomu ndi Gomora

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Woweruza wa Dziko Lonse Lapansi” Anawononga Sodomu ndi Gomora
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1988
  • Konzekerani Kaamba ka Chipulumutso Kuloŵa M’dziko Latsopano
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Muzikhulupirira “Woweruza wa Dziko Lonse Lapansi” Yemwe Ndi Wachifundo
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2024
  • Kumbukirani Mkazi wa Loti
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 February tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 18-19

“Woweruza wa Dziko Lonse Lapansi” Anawononga Sodomu ndi Gomora

18:23-25, 32; 19:24, 25

Kodi tikuphunzirapo chiyani pa zimene Yehova anachita ndi Sodomu komanso Gomora?

  • Yehova sadzalekerera zoipa ngakhale pang’ono

  • Anthu amene amamvera komanso kuchita zimene Mulungu amafuna ndi amene adzapulumuke chiweruzo chikubweracho.​—Luka 17:28-30

M’bale wachinyamata akukana pamene anthu ena akumuitana kuti akamwe mowa, kusuta komanso kutchova juga.

DZIFUNSENI KUTI: ‘Kodi ndimavutika mtima chifukwa cha khalidwe lotayirira la anthu a m’dzikoli?’ (2 Pet. 2:7) ‘Kodi zimene ndimachita tsiku lililonse zimasonyeza kuti ndimaona kuti kuchita chifuniro cha Yehova n’kofunika?’

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena