Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 4
  • May 11-17

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 11-17
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 4

May 11-17

GENESIS 38-39

  • Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Sanasiye Yosefe”: (10 min.)

    • Gen. 39:1​—Yosefe anakhala kapolo ku Iguputo (w14 11/1 12 ¶4-5)

    • Gen. 39:12-14, 20​—Yosefe anamunamizira ndipo anamutsekera m’ndende (w14 11/1 14-15)

    • Gen. 39:21-23​—Yehova anakhalabe ndi Yosefe (w14 11/1 15 ¶2)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 38:9, 10​—N’chifukwa chiyani Yehova anapha Onani? (it-2 555)

    • Gen. 38:15-18​—Kodi tinganene chiyani pa zimene Yuda ndi Tamara anachita? (w04 1/15 30 ¶4-5)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 38:1-19 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi, ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi mlongoyu anachita chiyani kuti uthenga wake ukhale womveka kwa mwininyumba? (th phunziro 17) Kodi wofalitsayu akanatani kuti agawire buku kapena magazini yopezeka pa Zinthu Zophunzitsira?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 2 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 1)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Sonyezani mmene mungayankhire munthu amene wanena zinthu zina zomwe anthu amakonda kunena ngati sakufuna kuti tikambirane nawo. (th phunziro 11)

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 3 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako musiyireni khadi lodziwitsa anthu za jw.org. (th phunziro 6)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 121

  • “Khalani Ngati Yosefe​—Thawani Dama”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Thawani Dama.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 84

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 54 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena