Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 4
  • Yehova Sanasiye Yosefe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Sanasiye Yosefe
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amatithandiza Kuti Zinthu Zizitiyendera Bwino
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • ‘Ndingachitirenji Choipa Chachikulu N’kuchimwira Mulungu?’
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Yehova Anapulumutsa Yosefe
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • ‘Kodi Mulungu Sindiye Amamasulira Maloto?’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 4
Yosefe ali m’ndende ku Iguputo.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | GENESIS 38-39

Yehova Sanasiye Yosefe

39:1, 12-14, 20-23

Pa nthawi imene Yosefe ankakumana ndi mayesero osiyanasiyana, Yehova ankadalitsa “chilichonse chimene anali kuchita” ndipo “anachititsa mkulu wa ndende kum’konda Yosefe.” (Gen. 39:2, 3, 21-23) Kodi nkhaniyi ikutiphunzitsa chiyani?

  • Tikakumana ndi mayesero tisamaganize kuti Yehova sakusangalala nafe.​—Sal. 34:19

  • Tiyenera kuyesetsa kuzindikira mmene Yehova akutidalitsira, n’kumamuyamikira.​—Afil. 4:6, 7

  • Tizidalira Yehova kuti azitithandiza.​—Sal. 55:22

Chithunzi choyamba: M’bale ali m’ndende ndipo akuwerenga kalata yomwe yachokera kwa anthu a m’banja lake. Chachiwiri: M’bale ali m’chipatala.
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena