Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 5
  • May 18-24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 18-24
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 5

May 18-24

GENESIS 40-41

  • Nyimbo Na. 8 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yehova Anapulumutsa Yosefe”: (10 min.)

    • Gen. 41:9-13​—Farao anamva kuti Yosefe akhoza kumasulira maloto (w15 2/1 14 ¶4-5)

    • Gen. 41:16, 29-32​—Yehova anathandiza Yosefe kumasulira maloto a Farao (w15 2/1 14-15)

    • Gen. 41:38-40​—Yosefe anakhala wachiwiri kwa Farao monga wolamulira ku Iguputo (w15 2/1 15 ¶3)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 41:14​—N’chifukwa chiyani Yosefe anameta asanakakumane ndi Farao? (w15 11/1 9 ¶1-3)

    • Gen. 41:33​—Kodi tingaphunzire chiyani tikaona mmene Yosefe analankhulira ndi Farao? (w09 11/15 28 ¶14)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 40:1-23 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Woyamba: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi, ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: N’chiyani chikusonyeza kuti banjali linakonzekera limodzi ulendo wobwerezawu? Kodi m’bale uja anatani pofuna kuthandiza mwininyumba kumvetsa bwino mfundo ya palemba lomwe anawerenga?

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 4 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. (th phunziro 11)

  • Ulendo Wobwereza Woyamba: (Osapitirira 5 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza woyamba. Kenako mugawireni buku kapena magazini yopezeka pa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 13)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 128

  • Khalani Ngati Yosefe​—Uzipilira Ngakhale Ena Akukuchitira Nkhanza: (6 min.) Yambani ndi kuonera vidiyo yakuti Khalani Bwenzi la Yehova​—Uzipilira Ngakhale Ena Akukuchitira Nkhanza. Kenako uzani ana omwe munawasankhiratu kuti abwere kupulatifomu ndipo afunseni mafunso awa: Kodi Kalebe ndi Sofiya anakumana ndi nkhanza zotani? Kodi mukuganiza kuti anaphunzira chiyani pa zimene zinachitikira Yosefe?

  • Zofunika Pampingo: (9 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 85

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 74 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena