Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 May tsamba 6
  • May 25-31

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • May 25-31
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 May tsamba 6

May 25-31

GENESIS 42-43

  • Nyimbo Na. 120 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Yosefe Anasonyeza Kudziletsa Kwambiri”: (10 min.)

    • Gen. 42:5-7​—Yosefe anakhala wodekha ataona azichimwene ake (w15 5/1 13 ¶5; 14 ¶1)

    • Gen. 42:14-17​—Yosefe anayesa azichimwene ake (w15 5/1 14 ¶2)

    • Gen. 42:21, 22​—Azichimwene ake a Yosefe anasonyeza mtima wolapa (it-2 108 ¶4)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Gen. 42:22, 37​—Kodi ndi makhalidwe abwino ati amene Rubeni anasonyeza? (it-2 795)

    • Gen. 43:32​—N’chifukwa chiyani Aiguputo ankaona kuti kudya pamodzi ndi Aheberi kunali konyansa? (w04 1/15 29 ¶1)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Gen. 42:1-20 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi, ndipo kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi m’bale uja ananena zotani zomwe zinali zogwirizana ndi lemba lomwe amafuna kuwerenga? Kodi m’bale uja anatani kuti agawire buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa ndipo n’chifukwa chiyani?

  • Ulendo Wobwereza Wachiwiri: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza wachiwiri. (th phunziro 15)

  • Phunziro la Baibulo: (Osapitirira 5 min.) lvs 38-39 ¶18 (th phunziro 8)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 94

  • “Muziyesetsa Kumvetsa Nkhani Yonse”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani mbali ina ya vidiyo yakuti Muziyesetsa Kumvetsa Zimene Mumawerenga M’Baibulo. Limbikitsani onse kuti akaonere vidiyo yonse kunyumba kwawo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 86 ndime 1-7

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 130 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena