Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 July tsamba 4
  • July 20-26

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • July 20-26
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 July tsamba 4

July 20-26

EKISODO 10-11

  • Nyimbo Na. 65 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Mose ndi Aroni Anasonyeza Kulimba Mtima Kwambiri”: (10 min.)

    • Eks 10:3-6​—Mose ndi Aroni anauza Farao molimba mtima za mliri wa 8 (w09 7/15 20 ¶6)

    • Eks 10:24-26​—Mose ndi Aroni anakana kumvera Farao

    • Eks 10:28; 11:4-8​—Mose ndi Aroni anauza Farao mopanda mantha za mliri wa 10 (it-2 436 ¶4)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 10:1, 2​—Kodi makolo angaphunzire chiyani pa mavesiwa? (w95 9/1 11 ¶11)

    • Eks 11:7​—Kodi Yehova ankatanthauza chiyani pamene ananena kuti “galu sadzauwa aliyense wa ana a Isiraeli”? (it-1 783 ¶5)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 10:1-15 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani mafunso otsatirawa: Kodi mwaphunzira chiyani pa zimene wofalitsayu anakambirana ndi mwininyumba? Kodi wofalitsayu akanatani kuti agawire buku kapena kabuku kopezeka pa Zinthu Zophunzitsira?

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako muitanireni kumisonkhano yathu. (th phunziro 8)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako mugawireni buku kapena kabuku kopezeka pa Zinthu Zophunzitsira. (th phunziro 12)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 55

  • “Kodi Zinthu za M’chilengedwe Zimatiphunzitsa Chiyani pa Nkhani ya Kulimba Mtima?”: (15 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Phunzirani Kulimba Mtima Kuchokera ku Zinthu za M’chilengedwe.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 92

  • Mfundo Zimene Taphunzira Komanso za Mlungu Wamawa (3 min.)

  • Nyimbo Na. 43 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena