Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 August tsamba 6
  • August 17-23

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • August 17-23
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 August tsamba 6

August 17-23

EKISODO 17-18

  • Nyimbo Na. 79 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Amuna Odzichepetsa Amaphunzitsa Ena N’kumawapatsa Zochita”: (10 min.)

    • Eks 18:17, 18​—Yetero anazindikira kuti Mose anali ndi udindo waukulu (w13 2/1 6)

    • Eks 18:21, 22​—Yetero analimbikitsa Mose kuti apereke ntchito zina kwa amuna ena oyenerera (w03 11/1 6 ¶1)

    • Eks 18:24, 25​—Mose anatsatira malangizo a Yetero (w02 5/15 25 ¶6)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 17:11-13​—Kodi tingatsanzire bwanji Aroni ndi Hura amene anachita zinthu mwamsanga kuti athandize Mose? (w16.09 6 ¶14)

    • Eks 17:14​—N’chifukwa chiyani mabuku amene Mose analemba ali m’gulu la mabuku ovomerezeka a m’Baibulo? (it-1 406)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 17:1-16 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Wobwereza: (5 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: Kodi tikuphunzira chiyani pa mmene Linda anayankhira Jamie atanena maganizo ake pa zimene zimachitika munthu akamwalira? Kodi Linda anachita chiyani pofuna kusonyeza kuti mfundo yapalembali ndi yothandiza?

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 3 min.) Gwiritsani ntchito chitsanzo cha ulendo wobwereza. (th phunziro 12)

  • Ulendo Wobwereza: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo wobwereza. Kenako gawirani buku la Zimene Baibulo Limaphunzitsa, ndipo yambitsani phunziro la Baibulo pogwiritsa ntchito mutu 6.(th phunziro 7)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 31

  • Zofunika Pampingo: (15 min.)

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) jy mutu 96

  • Mawu Omaliza (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 136 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena