Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 31
  • Muziyenda Ndi Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muziyenda Ndi Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova
  • “Muzitsimikizira Kuti Zinthu Zofunika Kwambiri Ndi Ziti”
    Imbirani Yehova
  • “Muzitha Kusankha Zinthu Zimene Ndi Zofunikadi Kwambiri”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • O Yendani ndi Mulungu!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 31

NYIMBO 31

Muziyenda Ndi Mulungu

Losindikizidwa

(Mika 6:8)

  1. 1. Muziyenda ndi Mulungu.

    Musonyeze chikondi

    Ndipo musachoke kwa Yehova,

    Azikulimbitsani.

    Muzimvera mawu akewo

    Simudzasochera

    Ndipo mukamamumvera

    Akutsogolerani.

  2. 2. Muziyenda ndi Mulungu.

    Muzipewa zoipa.

    Mayesero angakule bwanji

    Adzakuthandizani.

    Zinthu zonse zotamandika

    Ndiponso zoona

    Muziziganizirabe.

    M’lungu sakusiyani.

  3. 3. Muziyenda ndi Mulungu.

    Mudzasangalaladi.

    Muzimuthokoza pa zabwino

    Zomwe amapereka.

    Muimbireni M’lungu wathu,

    Inde, mwachimwemwe.

    Chimwemwecho ndi umboni

    Woti ndinu a M’lungu.

(Onaninso Gen. 5:​24; 6:9; Afil. 4:8; 1 Tim. 6:​6-8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena