Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb20 October tsamba 2
  • October 5-11

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • October 5-11
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
mwb20 October tsamba 2

October 5-11

EKISODO 31-32

  • Nyimbo Na. 45 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Thawani Kulambira Mafano”: (10 min.)

    • Eks 32:1​—Kulambira milungu yonyenga ndi kolakwika ngakhale pa nthawi yovuta (w09 5/15 11 ¶11)

    • Eks 32:4-6​—Aisiraeli anasakaniza kulambira Yehova ndi kulambira milungu yonyenga (w12 10/15 25 ¶12)

    • Eks 32:9, 10​—Yehova anakwiyira kwambiri Aisiraeli (w18.07 20 ¶14)

  • Kufufuza Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Eks 31:17​—Kodi Yehova wakhala akupuma pa tsiku la 7 lolenga zinthu m’njira iti? (w19.12 3 ¶4)

    • Eks 32:32, 33​—Kodi tikudziwa bwanji kuti si zoona kuti munthu akangolandira Yesu kukhala mpulumutsi wake ndiye kuti basi wapulumuka? (w87 9/1 29)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (Osapitirira 4 min.) Eks 32:15-35 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Vidiyo ya Ulendo Woyamba: (4 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi kenako funsani omvera mafunso otsatirawa: N’chifukwa chiyani tinganene kuti Brenda anagwiritsa ntchito bwino mafunso? Kodi anachita zotani pokonza zoti adzakambiranenso ndi munthuyo ulendo wotsatira?

  • Ulendo Woyamba: (Osapitirira 4 min.) Yambani ndi chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako musonyezeni ndi kukambirana naye mfundo za m’vidiyo yakuti N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? (koma musaonetse vidiyoyi). (th phunziro 9)

  • Nkhani: (Osapitirira 5 min.) w10 5/15 21​—Mutu: N’chifukwa Chiyani Yehova Sanalange Aroni Atapanga Fano la Mwana wa Ng’ombe? (th phunziro 7)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 36

  • “Muziona Kuti Ubwenzi Wanu Ndi Yehova Ndi Wamtengo Wapatali”: (15 min.) Nkhani Yokambirana. Onerani vidiyo yakuti Muziteteza Ubwenzi Wanu ndi Yehova (Akl 3:5).

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (Osapitirira 30 min.) jy mutu 103

  • Mawu Omaliza (Osapitirira 3 min.)

  • Nyimbo Na. 92 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena