Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 January tsamba 2
  • Pitirizani Kukhala Ndi Makhalidwe Oyera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizani Kukhala Ndi Makhalidwe Oyera
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Pitirizani Kusonyeza Kuti Mumakonda Kwambiri Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Yehova Amafuna Kuti Anthu Ake Azikhala Osiyana ndi Ena
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zikondwerero Zomwe Zimatikhudza
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Kodi Mukukumbukira?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 January tsamba 2
Bambo akuyang’ana kumbali chifukwa choipidwa ndi zimene zabwera pakompyuta yake ndipo akutseka kompyutayo.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Pitirizani Kukhala Ndi Makhalidwe Oyera

Yehova amafuna kuti tizikhala osiyana ndi anthu a m’dzikoli (Le 18:3; w19.06 27 ¶10)

Yehova amadana ndi machimo monga kugonana kwa pachibale, kwa amuna kapena akazi okhaokha komanso kugonana ndi nyama (Le 18:​6, 22, 23; w17.02 20 ¶13)

Yehova adzawononga anthu onse amene amachita makhalidwe oipa (Le 18:​24, 25; Miy 2:22; w14 7/1 7 ¶2)

Satana safuna kuti tidzalowe m’dziko latsopano. Koma mfundo za Yehova zingatiteteze ku msampha uliwonse wa Satana.

Kodi tingamusonyeze bwanji Yehova kuti timadana ndi makhalidwe oipa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena