Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 May tsamba 5
  • “Chikondi . . . Chimayembekezera Zinthu Zonse”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chikondi . . . Chimayembekezera Zinthu Zonse”
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Tizitsanzira Atumiki a Yehova Amene Anali Okhulupirika
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2016
  • “Pitirizani Kusonyeza Chikondi”
    Yandikirani Yehova
  • “Chikondi . . . Sichidzikuza”
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Yembekezani Yehova Kuti Mukhale Olimba Mtima
    Nsanja ya Olonda—2006
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 May tsamba 5

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

“Chikondi . . . Chimayembekezera Zinthu Zonse”

Chikondi chimatithandiza kuti tizifunira zabwino abale athu. (1Ak 13:4, 7) Mwachitsanzo, ngati m’bale kapena mlongo wachimwa n’kupatsidwa uphungu timayembekezera kuti autsatira ndipo asintha. Timaleza mtima ndi anthu omwe ali ndi chikhulupiriro chofooka ndipo timayesetsa kuwathandiza. (Aro 15:1) Ngati wina wasiya kusonkhana ndi mpingo, sitimataya mtima koma timayembekezera kuti tsiku lina adzabwerera.​—Lu 15:17, 18.

ONERANI VIDIYO YAKUTI MUZIKUMBUKIRA ZIMENE CHIKONDI CHIMACHITA KOMANSO ZIMENE SICHICHITA​—CHIMAYEMBEKEZERA ZINTHU ZONSE, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

  • Kodi Abineri anasintha bwanji?

  • Kodi Davide komanso Yowabu anachita bwanji zinthu ndi pempho la Abineri?

  • N’chifukwa chiyani tiyenera kuyembekezera zabwino kuchokera kwa abale athu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena