Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 6
  • November 27–December 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • November 27–December 3
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 6

November 27–December 3

YOBU 20-21

  • Nyimbo Na. 38 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Chuma Sichipangitsa Munthu Kukhala Wolungama”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Yob 20:2—Kodi akulu angathandize bwanji anthu amene akulimbana ndi ‘maganizo osautsa’? (w95 1/1 9 ¶19)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yob 20:​1-22 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (2 min.) Gwiritsani ntchito nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 1)

  • Ulendo Wobwereza: (5 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni kabuku kakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, ndipo musonyezeni mmene phunziro la Baibulo limachitikira. (th phunziro 6)

  • Nkhani: (5 min.) g 5/09 12-13—Mutu: Kodi Mulungu Amafuna Kuti Mukhale Wolemera? (th phunziro 17)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 136

  • “Mukhale Okhutira Ndi Zimene Muli Nazo Panopa”: (15 min.) Nkhani yokambirana komanso vidiyo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) bt mutu 2 ¶16-23

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 103 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena