Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 6
  • Chuma Sichipangitsa Munthu Kukhala Wolungama

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chuma Sichipangitsa Munthu Kukhala Wolungama
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amasangalala Tikamapempherera Ena
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Yobu Anapirira—Nafenso Tingatero!
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Yobu Afupidwa Chifukwa Chokhulupirika
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Mphotho ya Yobu—Magwero a Chiyembekezo
    Nsanja ya Olonda—1994
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Chuma Sichipangitsa Munthu Kukhala Wolungama

Zofari ananena kuti Mulungu amalanda chuma anthu oipa ndipo pamenepa ankasonyeza kuti Yobu ayenera kuti anachimwa (Yob 20:​5, 10, 15)

Yobu anayankha kuti: ‘N’chifukwa chiyani oipa zimawayendera?’ (Yob 21:​7-9)

Chitsanzo cha Yesu chimasonyeza kuti anthu olungama akhoza kukhala osauka (Lu 9:58)

M’bale akuwerengera lemba banja lina panja pa nyumba yawo. Bambo wa nyumbayo akutsatira m’Baibulo lake ndipo mkazi wake ndi mwana wawo wamng’ono akumvetsera mwachidwi.

FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi munthu wolungama amaona kuti chofunika kwambiri pa moyo wake n’chiyani, kaya akhale wolemera kapena wosauka?—Lu 12:21; w07 8/1 29 ¶12.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena