Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 12
  • December 18-24

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • December 18-24
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 12

December 18-24

YOBU 28-29

  • Nyimbo Na. 39 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • “Kodi Muli ndi Mbiri Ngati ya Yobu?”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Yob 29:24—Kodi tingaphunzire chiyani pa chitsanzo cha Yobu? (g00 7/8 29 ¶3)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yob 28:​1-28 (th phunziro 5)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

  • Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Mugawireni kabuku ka Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale. (th phunziro 3)

  • Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Mugawireni kabuku ka Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale, kenako kambiranani mwachidule mbali yakuti “Zimene Mungachite Kuti Muzipindula ndi Phunziro Lililonse.” (th phunziro 17)

  • Phunziro la Baibulo: (5 min.) lff phunziro 13 mawu oyamba a pa Fufuzani Mozama ndi mfundo 4 (th phunziro 6)

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

  • Nyimbo Na. 121

  • “Zochita Zanga Zimathandiza Kuti Gulu Lathu Likhale ndi Mbiri Yabwino”: (15 min.) Nkhani yokambirana komanso vidiyo.

  • Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) bt mutu 3 ¶12-18

  • Mawu Omaliza (3 min.)

  • Nyimbo Na. 50 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena