Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 March tsamba 6-16
  • March 24-30

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 24-30
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 March tsamba 6-16

MARCH 24-30

MIYAMBO 6

Nyimbo Na. 11 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

1. Kodi Tingaphunzire Chiyani kwa Nyerere?

(10 min.)

Tingaphunzire zambiri kuchokera kwa nyerere (Miy 6:6)

Ngakhale kuti zilibe wozilamulira, mwachibadwa nyerere zimagwira ntchito mwakhama, zimachita zinthu mogwirizana komanso zimakonzekereratu zam’tsogolo (Miy 6:7, 8; it-1 115 ¶1-2)

Muzitengera chitsanzo cha nyerere (Miy 6:9-11; w00 9/15 26 ¶3-4)

Nyerere zanyamula masamba.

© Aerial Media Pro/Shutterstock

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 6:16-19—Kodi machimo amene atchulidwa m’mavesi amenewa akutchula zinthu zonse zimene Yehova amadana nazo? (w00 9/15 27 ¶3)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 6:1-26 (th phunziro 10)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Woyamba

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Itanirani wachibale amene anasiya kusonkhana kuti adzamvetsere nawo nkhani yapadera komanso kuti adzabwere ku Chikumbutso. (lmd phunziro 4 mfundo 3)

5. Ulendo Woyamba

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Pemphani abwana anu kuti akuloleni kuti musadzapite kuntchito n’cholinga choti mudzapezeke pa Chikumbutso. (lmd phunziro 3 mfundo 3)

6. Ulendo Woyamba

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Muitanireni ku nkhani yapadera komanso ku Chikumbutso. (lmd phunziro 5 mfundo 3)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 2

7. Chilengedwe Chimasonyeza Kuti Yehova Amafuna Tizisangalala—Nyama Zochititsa Chidwi

(5 min.) Nkhani yokambirana.

Onerani VIDIYO. Kenako funsani funso lotsatirali:

  • Kodi zinyama zimatiphunzitsa chiyani zokhudza Yehova?

8. Zofunika Pampingo

(10 min.)

9. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 24 ¶7-12, bokosi patsamba 193

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 126 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena