Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb25 March tsamba 7
  • March 31–April 6

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • March 31–April 6
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Kabuku ka Msonkhano—2025
mwb25 March tsamba 7

MARCH 31–APRIL 6

MIYAMBO 7

Nyimbo Na. 34 ndi Pemphero | Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Hule wa nthawi yakale waima pakhomo la nyumba yake pamene mnyamata akudutsa chapafupi.

1. Muzipewa Zochitika Zimene Zingakuikeni M’mayesero

(10 min.)

Mnyamata wosadziwa zinthu anapita mwadala kukayendayenda m’dera limene mumakhala mahule (Miy 7:7-9; w00 11/15 29 ¶5)

Hule akubwera kudzakumana naye kuti amukope (Miy 7:10, 13-21; w00 11/15 30 ¶4-6)

Iye akukumana ndi mavuto chifukwa chodziika m’mayesero mwadala (Miy 7:22, 23; w00 11/15 31 ¶2)

2. Mfundo Zothandiza

(10 min.)

  • Miy 7:3—Kodi kumanga malamulo a Mulungu kuzala zathu komanso kuwalemba pamtima pathu kumatanthauza chiyani? (w00 11/15 29 ¶1)

  • Kodi ndi mfundo ziti zimene mwapeza pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno?

3. Kuwerenga Baibulo

(4 min.) Miy 7:6-20 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

4. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KUNYUMBA NDI NYUMBA. Pa ulendo wapita, munthuyo analandira kapepala komuitanira ku Chikumbutso ndipo anasonyeza chidwi. (lmd phunziro 9 mfundo 5)

5. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA MWAMWAYI. Pamene munkalankhula ndi munthuyo pa ulendo wapita, analandira kapepala komuitanira ku Chikumbutso ndipo anasonyeza chidwi. (lmd phunziro 9 mfundo 4)

6. Ulendo Wobwereza

(4 min.) KULALIKIRA M’MALO OPEZEKA ANTHU AMBIRI. Pamene munkalankhula ndi munthuyo pa ulendo wapita, analandira kapepala komuitanira ku Chikumbutso ndipo anasonyeza chidwi. (lmd phunziro 9 mfundo 3)

MOYO WATHU WA CHIKHRISTU

Nyimbo Na. 13

7. Mpaka Nthawi Ina Yabwino (Lu 4:6)

(15 min.) Nkhani yokambirana.

Onerani VIDIYO. Kenako funsani mafunso otsatirawa:

  • Kodi Yesu anayesedwa bwanji, nanga ifeyo tingakumanenso bwanji ndi mayesero ofanana ndi amenewa?

  • Kodi tingakane bwanji mayesero a Mdyerekezi?

8. Phunziro la Baibulo la Mpingo

(30 min.) bt mutu 24 ¶13-21

Mawu Omaliza (3 min.) | Nyimbo Na. 70 ndi Pemphero

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena