Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g02 3/8 tsamba 1-3
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2002
  • Nkhani Yofanana
  • Mavuto a Uphunzitsi
    Galamukani!—2002
  • N’kusankhiranji Uphunzitsi?
    Galamukani!—2002
  • Mafunso Ochokera kwa Oŵerenga
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Uphunzitsi Uli M’pokomera Pake
    Galamukani!—2002
Onani Zambiri
Galamukani!—2002
g02 3/8 tsamba 1-3

Zamkatimu

March 8, 2002

Kodi Tidakatani Padakapanda Aphunzitsi?

N’zotheka kuti pamagulu onse a anthu amene amagwira ntchito padziko lonse, aphunzitsi ndiwo ochuluka kwambiri. Tonsefe tinafika pamene tilipa chifukwa cha khama lawo potiphunzitsa. Koma kodi n’zinthu zotani zimene zimavuta ndiponso kusangalatsa pophunzitsa?

3 N’Chifukwa Chiyani Timafunikira Aphunzitsi?

5 N’kusankhiranji Uphunzitsi?

7 Mavuto a Uphunzitsi

12 Uphunzitsi Uli M’pokomera Pake

14 Lingaliro la Baibulo

Kodi Kudziona Ngati Wolakwa N’koipa Nthaŵi Zonse?

20 Achinyamata Akufunsa Kuti . . .

Kodi Zingakhale Bwanji Ngati Nditakumana ndi Winawake wa Kusukulu Kwathu?

23 Zochititsa Kuti Kuntchito Kukhale Koopsa

24 Kukhala Otetezeka Kumalo Anu Antchito

27 Malingaliro Oyenera a Ntchito

20 Kodi Mdyerekezi Alikodi?

31 Uchi—Mankhwala Ozuna

32 Mmene Anapezera Mphoto Yoyamba

Amasai—Anthu Odabwitsa Ndiponso Ochititsa Kaso 16

Moyo wa anthu okongola ameneŵa amene amakhala m’chigawo cha Kummaŵa kwa Africa muchita nawo chidwi kwambiri.

[Mawu a Chithunzi patsamba 3]

COVER: UNITED NATIONS/RAY WITLIN

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena