Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g04 4/8 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2004
  • Nkhani Yofanana
  • Mmene Moyo wa Mose Umakukhudzirani
    Galamukani!—2004
  • Mose Anali Munthu Wachikondi
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Mose Anali Ndani?
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Kodi Ndimotani Mmene Yesu Kristu Analiri Mneneri Wofanana ndi Mose?
    Nsanja ya Olonda—1991
Onani Zambiri
Galamukani!—2004
g04 4/8 tsamba 1-2

Zamkatimu

April 8, 2004

Kodi Dzikoli Lingasinthidwe Kuti Likhale Labwino?

Anthu ambiri amaona kuti zinthu zambiri padziko pano, kuphatikizapo moyo wa anthu n’zofunika zitasintha kwabasi. Koma kodi akuluakulu ofuna kusintha zinthu angakwanitse kutero? Ngati iwoŵa sangatero, ndani amene angakwanitse?

3 Kufunitsitsa Kusintha Zinthu

5 Kodi Anthu Ofuna Kusintha Zinthu Angakwanitse Kutero?

11 Chinthu Chabwino Koposa Kusintha Kotereku

18 Anapulumuka Madzi Atasefukira!

19 Kusamvana Pankhani ya Mose

20 Kodi Mose Anali Munthu Weniweni Kapena Wongopeka?

26 Mmene Moyo wa Mose Umakukhudzirani

30 Lingaliro la Baibulo

Kodi n’zotheka Kusiya Zizoloŵezi Zoipa?

32 Tsiku Lofunika Kulikumbukira Lamlungu pa April 4, 2004

N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Tizivutika? 12

Kodi tiyenera kumupsera mtima Mulungu chifukwa cholola kuti tizivutika? Onani yankho logwira mtima la funsoli lomwe lili m’Baibulo.

Sungani Nthaŵi! 15

Vuto la kuchedwa lingasokoneze kwambiri moyo ndiponso ntchito ya munthu. Naŵa malangizo ena amene angakuthandizeni kusunga nthaŵi.

[Mawu a Chithunzi patsamba 2]

COVER: Globe: Used with permission from The George F. Cram Company, Indianapolis, Indiana

UN/DPI Photo by Eskinder Debebe

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena