Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 12/10 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Galamukani!—2010
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Krisimasi Imatanthauzanji kwa Inu?
    Nsanja ya Olonda—1994
  • Miyambo ya Krisimasi—Kodi Ziyambi Zake Nzotani?
    Galamukani!—1989
  • Krisimasi—kodi Nchifukwa Ninji Iri Yotchuka Kwambiri M’japani?
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Chiyambi cha Krisimasi Yamakono
    Nsanja ya Olonda—1997
Onani Zambiri
Galamukani!—2010
g 12/10 tsamba 1-2

Zamkatimu

December 2010

Kodi Khirisimasi Inayamba Bwanji?

Werengani nkhanizi kuti muone mmene kudziwa chiyambi cha Khirisimasi kwathandizira mabanja ena.

3 N’chifukwa Chiyani Anthu Ambiri Akukondwerera Khirisimasi Masiku Ano?

5 Kodi Khirisimasi Inayamba Bwanji?

8 “Choonadi Chidzakumasulani”

12 Mulungu Wanditonthoza M’mayesero Anga Onse

20 Tiyembekezere Zivomezi Zinanso Zikuluzikulu

22 Zimene Achinyamata Amadzifunsa

Kodi Ndingafotokoze Bwanji Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani Yogonana Amuna Kapena Akazi Okhaokha?

25 Panagona Luso!

Nsomba za Salimoni Zimasambira Mogometsa

26 Buku Limene Mungathe Kulikhulupirira—Gawo 2

Zimene Baibulo Limanena Zokhudza Ufumu wa Asuri

29 Zochitika Padzikoli

30 Mlozera Nkhani wa Magazini a Galamukani! a 2010

31 Zoti Banja Likambirane

32 Ankaphunzirira Limodzi ndi Ana Ake

Bwanji Mulungu Osangomuwononga Mdyerekezi? 10

Baibulo limatitsimikizira kuti Mulungu adzawononga Satana pa nthawi yoyenerera. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chifukwa chake sanamuwonongebe mpaka pano.

Chivomezi cha ku Haiti Chinapereka Mpata Wosonyeza Chikhulupiriro ndi Chikondi 14

Chivomezi chimene chinachitika ku Haiti mu January 2010 chinagwetsa nyumba zambiri komanso kupha anthu oposa 200,000. Werengani nkhaniyi kuti mumve mmene anthu anadziperekera kuti athandize anthu okhudzidwa ndi chivomezichi komanso mmene anapulumutsira anthu ndi kuwapatsa chiyembekezo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena