Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g18 No. 1 tsamba 16
  • Dziwani Zambiri Zokhudza Zimene Tingachite Kuti Tizikhala Osangalala

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dziwani Zambiri Zokhudza Zimene Tingachite Kuti Tizikhala Osangalala
  • Galamukani!—2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • KODI MUNADZIFUNSAPO KUTI:
  • KUTI MUPEZE MAYANKHO A MAFUNSOWA KOMANSO ENA
  • Kodi Tingapeze Kuti Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambiri Okhudza Moyo?
    Kodi Mayankho a Mafunso Ofunika Kwambiri Okhudza Moyo Tingawapeze Kuti?
  • Kodi Munayamba Mwadzifunsapo?
    Galamukani!—2019
  • Mungaphunzirenso Izi
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Kachipangizo Kothandiza Kwambiri
    Kodi Zopereka Zanu Zimagwiritsidwa Ntchito Bwanji?
Onani Zambiri
Galamukani!—2018
g18 No. 1 tsamba 16
Kupeza mayankho pa jw.org

MUNGATANI KUTI MUZIKHALA WOSANGALALA?

Dziwani Zambiri

KODI MUNADZIFUNSAPO KUTI:

  • Ndingatani kuti banja langa lizisangalala?

  • Ndingatani kuti ndipeze anzanga abwino komanso kuti ena azindiona kuti ndine munthu wabwino?

  • Kodi anthu amene anamwalira adzakhalanso ndi moyo?

  • Kodi mavuto amene timakumana nawowa adzathadi?

  • Kodi anthu sadzaliwonongeratu dziko lapansili?

  • Kodi zipembedzo zonse zimathandiza anthu kudziwa Mulungu woona?

KUTI MUPEZE MAYANKHO A MAFUNSOWA KOMANSO ENA

Pitani pawebusaiti yathu ya jw.org yomwe ikupezeka m’zinenero zoposa 900. Pamalowa mukhoza kupeza mfundo zothandiza kwambiri pa nkhani zosiyanasiyana.

Mungapezeponso mavidiyo a anthu osiyanasiyana omwe anayamba kusangalala ataphunzira Baibulo ndipo sakunong’oneza bondo. Ena mwa anthuwa ankagwiritsa ntchito mankhwala osokoneza bongo ndipo ena anali akaidi. Enanso ndi ophunzira kwambiri kuphatikizaponso akatswiri a zasayansi.

Pa jw.org/ny mukhoza kuwerenga kapena kupanga dawunilodi Mabaibulo komanso mabuku ndi magazini osiyanasiyana, kwaulere. Nkhani zina zomwe mungazipeze pawebusaiti ndi izi:

  • Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala

  • Kodi Mungatani Kuti Muzisangalala?

  • Uthenga Wabwino Wochokera kwa Mulungu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena