Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 10
  • Khalani Okhazikika, Osasunthika!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Okhazikika, Osasunthika!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Olimba, Osasunthika
    Imbirani Yehova
  • Khalani Olimba Komanso Osasunthika
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Pitirizanibe Kufunafuna Ufumu Choyamba
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 10

Nyimbo 10

Khalani Okhazikika, Osasunthika!

(1 Akorinto 15:58)

1. Popeza ‘masiku ngomaliza,’

Tifulumire muntchito yathu.

Tikhaletu osagwedezeka,

Ndi okhulupirika (mutumiki).

(Korasi)

2. Zosangalatsa m’dziko nzambiri.

Tikhale olama maganizo.

Ngati tikhazikika kwa M’lungu,

Adzatitetezera. (nthaŵi zonse).

(Korasi)

3. Tiyeni titumikire M’lungu.

Tigalamuke tisawodzere.

Tigwiritsitse Mbiri Yabwino.

Masikuwa adzatha. (posachedwa).

(KORASI)

Tiyenera kulimba; Tisiyane ndi dziko,

Tidye chowonadi tisunge umphumphu.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena