Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 32
  • Khalani Olimba, Osasunthika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khalani Olimba, Osasunthika
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Okhazikika, Osasunthika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Khalani Olimba Komanso Osasunthika
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Pitirizani Kutumikira Yehova ndi Mtima Wokhazikika
    Nsanja ya Olonda—2002
  • Khalani Okhazikika Kuti Mudzapambane pa Mpikisano wa Moyo
    Nsanja ya Olonda—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 32

Nyimbo 32

Khalani Olimba, Osasunthika

Losindikizidwa

(1 Akorinto 15:58)

1. Anthu akuvutika kwambiri.

Poopa zinthu zili m’tsogolo.

Tikhale osasunthika konse,

Potumikira M’lungu.

(KOLASI)

Tikhaletu olimba

Tisiyane ndi dziko.

Tidye choonadi,tikhulupirike.

2. Misampha ndi yambiri m’dzikoli.

Koma mwanzeru tingaipewe.

Tikakhulupirira Mulungu,

Adzatisamalira.

(KOLASI)

Tikhaletu olimba

Tisiyane ndi dziko.

Tidye choonadi,tikhulupirike.

3. Tilambire Yehova Mulungu,

Tim’tumikire mogwirizana.

Tilalike uthenga mwachangu,

Mapeto adzafika.

(KOLASI)

Tikhaletu olimba

Tisiyane ndi dziko.

Tidye choonadi,tikhulupirike.

(Onaninso Luka 21:9; 1 Pet. 4:7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena