Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 33
  • ‘Yehova Iye Mwini Wakhala Mfumu!’

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Yehova Iye Mwini Wakhala Mfumu!’
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova ndi Mfumu Yathu
    Imbirani Yehova
  • Yehova Ndi Mfumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Nyimbo kwa Wammwambamwambayo
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 33

Nyimbo 33

‘Yehova Iye Mwini Wakhala Mfumu!’

(Salmo 97:1)

1. Anthu, thokozani Yehova.

Lengezani zochita zakezo.

Imbirani Mulungu wathu mokondwa,

Eya, kuthiranso mang’ombe.

(Korasi)

2. Nena ulemerero wake.

Ndi chipulumutso apeleka.

Yehova ndiwamkulu atamandidwe

Koposa ndi milungu yonse.

(Korasi)

3. Mphamvu ndi kumveka nza M’lungu.

M’thokozeni kamba ka Mwana’ke.

M’malo oyera gwadirani Mulungu,

Nenani mokweza Yehova.

(KORASi)

Miyamba ikondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ali Mfumu!

Miyamba ikondwe, Dziko likondwere,

Chifukwa Yehova ali Mfumu!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena