Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 9
  • Yehova Ndi Mfumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Ndi Mfumu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova ndi Mfumu Yathu
    Imbirani Yehova
  • ‘Yehova Iye Mwini Wakhala Mfumu!’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Ufumu Umene Ukulamulira Kumwamba Ubwere
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 9

NYIMBO 9

Yehova Ndi Mfumu

Losindikizidwa

(Salimo 97:1)

  1. 1. Tizilemekeza Yehova,

    Ntchito zake zonse n’zachilungamo.

    Tiimbire Mulungu mosangalala,

    Tilalikire ntchito zake.

    (KOLASI)

    Kumwamba ndi dziko zisangalaletu

    Chifukwa Yehova ndi Mfumu.

    Kumwamba ndi dziko zisangalaletu

    Chifukwa Yehova ndi Mfumu.

  2. 2. Lalikira mitundu yonse

    Chifukwa M’lungu atipulumutsa.

    Titamande Yehova Mulungu wathu.

    Tiyenitu timulambire.

    (KOLASI)

    Kumwamba ndi dziko zisangalaletu

    Chifukwa Yehova ndi Mfumu.

    Kumwamba ndi dziko zisangalaletu

    Chifukwa Yehova ndi Mfumu.

  3. 3. Wakhazikitsatu Ufumu,

    Mwana wake ndiye wolamulira.

    Milungu yabodza

    ichite manyazi,

    Tilambire Yehova yekha.

    (KOLASI)

    Kumwamba ndi dziko zisangalaletu

    Chifukwa Yehova ndi Mfumu.

    Kumwamba ndi dziko zisangalaletu

    Chifukwa Yehova ndi Mfumu.

(Onaninso 1 Mbiri 16:9; Sal. 68:20; 97:​6, 7.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena