Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 65
  • Kusonkhana Muumodzi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kusonkhana Muumodzi
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Banja la Yehova Lili ndi Umodzi Wamtengo Wapatali
    Nsanja ya Olonda—1996
  • Kugwirira Ntchito Pamodzi m’Chigwirizano
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Kondwerani m’Chiyembekezo’
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Sungani Umodzi m’Masiku Ano Otsiriza
    Nsanja ya Olonda—1996
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 65

Nyimbo 65

Kusonkhana Muumodzi

(Salmo 133)

1. Nkokomatu kuwona

Abale pamodzi,

Kusonyeza chikondi

Kugwira mu’modzi!

Madalitso a Yehova

Ali ngati mame

Omagwera pa Ziyoni

Amaziziritsa.

2. Tisonkhane pamodzi;

Tilimbikitsane.

Kulengeza poyera

Chiyembekezocho.

Tiri achangu kukonza

Misonkhano yathu,

Tikhale okonzekera

Kupatsa Cho’nadi.

3. M’lungu wodalirika;

Mawu ake ngo’na.

Tiphunzire pamodzi

Za chiyembekezo.

Osaleka kusonkhana

Pamodzi abale,

Makamaka pakuwona

Tsiku liyandika.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena