Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 148
  • Kutamanda Mulungu Wathu Mfumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kutamanda Mulungu Wathu Mfumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Mudalitse Msonkhano Wathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Yehova Amafunikira Chitamando Chosatha
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Dalitsani Msonkhano Wathu!
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 148

Nyimbo 148

Kutamanda Mulungu Wathu Mfumu

(Salmo 145:1)

1. O imbirani Yehova!

Tamani Ya tsiku lonse.

Tisonyeze dzina lake

Tiyandikire kwa iye.

Afutukula dzanjalo

Ali chire kuthandiza.

Tikhale odalirika;

Yehova ngwachisomodi.

2. Choncho tikhulupirike

Tinene ‘Nditamandanu.’

Mulungu ngwachilungamo;

Titame ukulu wake.

Atchinjiriza omkonda;

Sikudzakhala kovuta.

Atithandiza m’mavuto.

Titame Yehova Mfumu.

3. Ufumu wayandikira

Kudzetsa zinthu zabwino.

Lengeza Ufumu konse,

Iwe ‘wokhutiritsidwa.’

Yehova waika Mfumu

Yosanyozedwa ndi munthu.

Oipa adzachotsedwa.

Kulamula kudzakhala.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena