Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 192
  • Kudziŵitsa Chowonadi Chaufumu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kudziŵitsa Chowonadi Chaufumu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tikulalikira Choonadi Chonena za Ufumu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tilalikire Choonadi cha Ufumu
    Imbirani Yehova
  • “Kunyumba ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 192

Nyimbo 192

Kudziŵitsa Chowonadi Chaufumu

(Machitidwe 20:20, 21)

1. Tinali osadziŵatu

Njira yoyenda Akristu.

Yehova anaŵalitsa,

Chowonadi Chaufumu.

2. Mwaŵi wathu tiwuwona

Kugwilira Teokrase,

Nenani mbiri ya M’lungu,

Chotero kumlemekeza.

3. Tilalikira kwa onse,

Panyumba ndi pakhwalala.

Timaphunzitsa anthu za

Chowonadi chomasula.

4. Tikuyesa kukulitsa

kulambira kowonako,

Titumikire momvana,

Kufikira ntchito ithe.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena