Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 223
  • Okhulupirika Anu Adzakulemekezani

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Okhulupirika Anu Adzakulemekezani
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova Amafunikira Chitamando Chosatha
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Chikondi Chokhulupirika cha Yehova N’chachikulu
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Kodi Timapindula Bwanji ndi Chikondi Chokhulupirika cha Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2021
  • Tizikhulupirika Nthawi Zonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 223

Nyimbo 223

Okhulupirika Anu Adzakulemekezani

(Salmo 145:10)

1. Okhulupirika anu

Yehova Mulungu.

Amalengezatu ntchito

Ndi ulemerero.

Muli wapamwamba,

Wotamandika zedi,

Zosasanthulika,

Ntchito zanu, njira zanu.

Okhulupirika anu;

Aimba mokondwa.

Afuna kuuza anthu

Zimene adziŵa.

2. Mulungu wasankha mbadwo

Kuti umtamande.

Mbadwowo tsono ulipo,

Woyenda ndi M’lungu.

Kapolo wakeyo,

Amadyetsa nkhosazo

Popyola m’dzikoli,

Mbusa wawo patsogolo.

Monga okhulupirika,

Atamanda dzina.

Amalengeza mokondwa

Za ukulu wanu.

3. Ya Mulungu ndiwabwino;

Sitikayikira.

Adzapulumutsa anthu

—Titame ukoma.

Amaleza mtima;

Anthu ake adziŵa.

Tiyamike zedi

Kuti atifuna ife!

Polefuka atidzutsa

Nakhutitsa mtima.

Timdalitsa tsiku lonse;

Timlemekezadi.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena