Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • jd tsamba 42
  • Dziwani Yehova Ndipo Mutumikireni

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dziwani Yehova Ndipo Mutumikireni
  • Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
  • Nkhani Yofanana
  • Uthenga Umene Yehova Anapereka Kalelo Ndi Wothandizanso Masiku Ano
    Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
  • Mulungu Angakuthandizeni Kukonzekera Tsiku Lake Lalikulu
    Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
  • Mfundo Yaikulu mu Uthenga wa Aneneri 12 Inali Yokhudza Tsiku la Yehova
    Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
  • Kuchita Zinthu ‘Mwachilungamo’ N’kofunika Kwambiri Kuti Timudziwe Mulungu
    Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
Onani Zambiri
Muzikumbukira Tsiku la Yehova Nthawi Zonse
jd tsamba 42
Chithunzi patsamba 42

GAWO 2

Dziwani Yehova Ndipo Mutumikireni

Kodi m’mabuku 12 a aneneri muli uthenga wotani, womwe ukutichititsa kuti tizifunitsitsa kumudziwa bwino kwambiri Yehova? N’chifukwa chiyani mauthenga a Yehova, omwe aneneriwa ankalengeza ali ofunika kwambiri masiku ano? Pamene mukuphunzira Mutu 4 mpaka 7 m’buku lino, mupeza malangizo okuthandizani kulambira Mulungu m’njira yoyenera. Komanso mupeza mfundo zokuthandizani kudziwa mmene mungagwiritsire ntchito mfundo za Mulungu za makhalidwe abwino. Mwachitsanzo, mudziwa zimene Mulungu amafuna kuti muzichita posonyeza kuti ndinu wachilungamo. Zoonadi, mabuku 12 aulosiwa, akuthandizani kuti mukhale ndi moyo wabwino masiku ano.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena