Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mb phunziro 3
  • Phunziro 3

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Phunziro 3
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
mb phunziro 3

Phunziro 3

Losindikizidwa

1 Petulo 3:8

Davide wamva zoti mnzake akudwala.

Choncho akunena kuti: “Ndadziwa chochita.

Ndimulembera kalata yomulimbikitsa, ndipo kenako ndikam’patsa.”

Uzisonyeza ena chifundo, ndipo nonse mudzakhala osangalala.

ZOTI MUCHITE

Mwana wanuyo muwerengereni:

1 Petulo 3:8

Muuzeni mwanayo kuti aloze:

Nyumba Tebulo Davide

Dzuwa Mbalame Mtengo

Mufunseni mwana wanu kuti:

Kodi ukudziwa aliyense amene akudwala?

Kodi tingamuthandize bwanji kuti achire?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena