Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 53
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Phunziro 3
    Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
  • Zimene Ndikuphunzira M’Baibulo
    Nsanja ya Olonda—2012
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 53

NYIMBO 53

Kukonzekera Kupita Kokalalikira

Losindikizidwa

(Yeremiya 1:17)

  1. 1. Tsopano

    Kunja kwacha

    Tikalalikiretu.

    Komano mvula

    Ikuyamba kugwa,

    N’zosavuta kupitiriza

    Kugona.

    (KOLASI)

    Tisafooke tikonzeke.

    Tipemphe Yehova

    Kuti azitilimbikitsa

    Pokonzeka.

    Tipezenso woyenda naye

    Wotilimbikitsa.

    Angelo atitsogolera

    Tikwanitsa.

  2. 2. Tipeza

    Chimwemwedi

    Ngati sitifooka.

    Ndipo Yehova

    Amaona zonse,

    Iye saiwala chikondi

    Chathuchi.

    (KOLASI)

    Tisafooke tikonzeke.

    Tipemphe Yehova

    Kuti azitilimbikitsa

    Pokonzeka.

    Tipezenso woyenda naye

    Wotilimbikitsa.

    Angelo atitsogolera

    Tikwanitsa.

(Onaninso Mlal. 11:4; Mat. 10:​5, 7; Luka 10:1; Tito 2:​14.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena