Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 10
  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tamandani Yehova Mulungu Wathu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tamandani Yehova, Mulungu Wathu!
    Imbirani Yehova
  • Tamandani Mwana Woyamba Kubadwa wa Yehova
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Imbani Chitamando cha Yehova Molimbika!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tamandani Mfumu Yatsopano Yolamulira Dziko Lapansi
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 10

NYIMBO 10

Tamandani Yehova Mulungu Wathu

Losindikizidwa

(Salimo 145:12)

  1. 1. Tamanda Yehova M’lungu.

    Phunzitsa za dzina lake.

    Chenjeza anthu adziwe

    Tsiku lake layandikira.

    Walamula kuti Mwana wake

    Akhale Mfumu padziko.

    Udziwitse mitundu ya anthu

    Kuti adzatidalitsa.

    (KOLASI)

    Tamanda Yehova M’lungu.

    Lengeza kuti ndi wamphamvu.

  2. 2. Tamanda Yehova M’lungu.

    Uimbe mosangalala.

    Sonyeza khama lakotu

    Polalikira anthu onse.

    Ngakhale Mulungu ndi wamphamvu,

    Iye amadzichepetsa.

    Ndi wachifundo chachikuludi,

    Amayankha mapemphero.

    (KOLASI)

    Tamanda Yehova M’lungu.

    Lengeza kuti ndi wamphamvu.

(Onaninso Sal. 89:27; 105:1; Yer. 33:11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena