Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 37
  • Kutumikira Yehova Ndi Moyo Wonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kutumikira Yehova Ndi Moyo Wonse
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tizitumikira Yehova ndi Moyo Wathu Wonse
    Imbirani Yehova
  • M’patseni Yehova Ulemerero
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Yehova Amayamikira Utumiki Wanu wa Mtima Wonse
    Nsanja ya Olonda—1997
  • Chikondi cha Mulungu Chokhulupirika
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 37

NYIMBO 37

Kutumikira Yehova Ndi Moyo Wonse

Losindikizidwa

(Mateyu 22:37)

  1. 1. Yehova Wamphamvuyonse

    Ineyo ndimakukondani.

    Ndikufuna n’kutumikireni

    Ndi mtima wanga wonse.

    Ndizimvera mawu anu ndi

    Kuchita zofuna zanu.

    (KOLASI)

    Inu Yehova ndinu woyenera

    Kutumikiridwa.

  2. 2. Atate zomwe munalenga

    Zimakulemekezani.

    Ndidzalengeza za inu

    Kwa ena mokhulupirika.

    Yehova muzindithandiza

    Kuti ndikhulupirike.

    (KOLASI)

    Inu Yehova ndinu woyenera

    Kutumikiridwa.

(Onaninso Deut. 6:15; Sal. 40:8; 113:​1-3; Mlal. 5:4; Yoh. 4:34.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena