Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 131
  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • “Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”
    Imbirani Yehova
  • Anthu Achimwemwe a Yehova
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Moyo Wosatha Ulonjezedwa
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 131

NYIMBO 131

“Chimene Mulungu Wachimanga Pamodzi”

Losindikizidwa

(Mateyu 19:​5, 6)

  1. 1. Chingwe cholimbadi

    Chamangidwa lero.

    Mulungu ndi anthufe

    Tamva malumbiro.

    (KOLASI 1)

    Mwamuna walumbira

    Kukonda mkaziyu.

    “Chomwe M’lungu wamanga,

    Musalekanitse.”

  2. 2. Onse afufuza

    M’Mawu a Mulungu,

    Kuti akwaniritse

    Zomwe alumbira.

    (KOLASI 2)

    Mkazinso walumbira

    Kukonda mwamuna.

    “Chomwe M’lungu wamanga,

    Musalekanitse.”

(Onaninso Gen. 2:24; Mla. 4:12; Aef. 5:​22-33.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena