Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm18 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2018
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • MASANA
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2017
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2018
CO-pgm18 tsamba 4-5

Loweruka

“[Kuonetsa] kulimba mtima kowonjezereka polankhula mawu a Mulungu mopanda mantha”​—AFILIPI 1:14

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 76 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Muzichita Zinthu Molimba Mtima

    • Amene Mukuphunzira Baibulo (Machitidwe 8:35, 36; 13:48)

    • Achinyamata (Salimo 71:5; Miyambo 2:11)

    • Ofalitsa (1 Atesalonika 2:2)

    • Amene Muli pa Banja (Aefeso 4:26, 27)

    • Makolo (1 Samueli 17:55)

    • Apainiya (1 Mafumu 17:6-8, 12, 16)

    • Akulu (Machitidwe 20:28-30)

    • Achikulire (Danieli 6:10, 11; 12:13)

  • 10:50 Nyimbo Na. 119 ndi Zilengezo

  • 11:00 NKHANI YOSIYIRANA: Musamatsanzire Anthu Amantha, Koma Olimba Mtima

    • Osati Atsogoleri 10, Koma Yoswa ndi Kalebe (Numeri 14:7-9)

    • Osati Anthu a ku Merozi, Koma Yaeli (Oweruza 5:23)

    • Osati Aneneri Onyenga, Koma Mikaya (1 Mafumu 22:14)

    • Osati Uliya, Koma Yeremiya (Yeremiya 26:21-23)

    • Osati Wolamulira Wachinyamata, Koma Paulo (Maliko 10:21, 22)

  • 11:45 NKHANI YA UBATIZO: “Ife Si Mtundu wa Anthu Obwerera M’mbuyo” (Aheberi 10:35, 36, 39; 11:30, 32-34, 36; 1 Petulo 5:10)

  • 12:15 Nyimbo Na. 38 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 111

  • 1:50 NKHANI YOSIYIRANA: Phunzirani Kulimba Mtima Kuchokera ku Zinthu za M’chilengedwe

    • Mikango (Mika 5:8)

    • Mahatchi (Yobu 39:19-25)

    • Msulu (Salimo 91:3, 13-15)

    • Choso (1 Petulo 3:15)

    • Njovu (Miyambo 17:17)

  • 2:40 Nyimbo Na. 60 ndi Zilengezo

  • 2:50 NKHANI YOSIYIRANA: Mmene Abale Athu Akusonyezera Kulimba Mtima

    • Ku Africa (Mateyu 10:36-39)

    • Ku Asia (Zekariya 2:8)

    • Ku Europe (Chivumbulutso 2:10)

    • Ku North America (Yesaya 6:8)

    • Ku Oceania (Salimo 94:14, 19)

    • Ku South America (Salimo 34:19)

  • 4:15 Olimba Mtima Koma Osati Odzidalira (Miyambo 3:5, 6; Yesaya 25:9; Yeremiya 17:5-10; Yohane 5:19)

  • 4:50 Nyimbo Na. 3 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena