Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm21 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Nkhani Yofanana
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2020
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lamlungu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2019
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2021
CO-pgm21 tsamba 4-5
Zithunzi: 1. Mlongo akucheza ndi ana ake. 2. Alongo awiri akulalikira m’dera lina lakumudzi ku Asia. 3. Danieli komanso anzake atatu a Chiheberi aima pamaso pa mfumu ya Babulo.

Loweruka

‘Menya mwamphamvu nkhondo yachikhulupiriro’​—Yuda 3

M’MAWA

  • 9:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 9:30 Nyimbo Na. 57 ndi Pemphero

  • 9:40 NKHANI YOSIYIRANA: Anthu Opanda Chikhulupiriro Akhoza Kusintha N’kukhala ndi Chikhulupiriro

    • • Anthu a ku Nineve (Yona 3:5)

    • • Abale Ake a Yesu (1 Akorinto 15:7)

    • • Anthu Otchuka (Afilipi 3:7, 8)

    • • Anthu Osapembedza (Aroma 10:13-15; 1 Akorinto 9:22)

  • 10:30 Muzilimbitsa Chikhulupiriro Chanu Pogwiritsa Ntchito Buku Lakuti Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale (Yohane 17:3)

  • 10:50 Nyimbo Na. 67 ndi Zilengezo

  • 11:00 NKHANI YOSIYIRANA: Anthu Omwe Apambana pa Nkhondo Yachikhulupiriro

    • • Amene Ali pa Banja Ndi Munthu Wosakhulupirira (Afilipi 3:17)

    • • Amene Akuleredwa Ndi Kholo Limodzi (2 Timoteyo 1:5)

    • • Akhristu Omwe Sali pa Banja (1 Akorinto 12:25)

  • 11:45 NKHANI YA UBATIZO: Kukhala Ndi Chikhulupiriro N’kofunika Kuti Tidzapeze Moyo Wosatha (Mateyu 17:20; Yohane 3:16; Aheberi 11:6)

  • 12:15 Nyimbo Na. 79 ndi Kupuma

MASANA

  • 1:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 1:45 Nyimbo Na. 24

  • 1:50 NKHANI YOSIYIRANA: Mmene Abale Athu Akusonyezera Chikhulupiriro ku . . .

    • • Africa

    • • Asia

    • • Europe

    • • North America

    • • Oceania

    • • South America

  • 2:15 NKHANI YOSIYIRANA: Lowani pa Khomo la Utumiki Mwachikhulupiriro

    • • Phunzirani Chilankhulo China (1 Akorinto 16:9)

    • • Samukirani Kumene Kukufunika Olalikira Ufumu Ambiri (Aheberi 11:8-10)

    • • Funsirani Sukulu ya Akhristu Olalikira za Ufumu (1 Akorinto 4:17)

    • • Thandizani pa Ntchito Yazomangamanga (Nehemiya 1:2, 3; 2:5)

    • • ‘Muziika Kenakake Pambali’ Kothandizira pa Ntchito ya Yehova (1 Akorinto 16:2)

  • 3:15 Nyimbo Na. 84 ndi Zilengezo

  • 3:20 VIDIYO: Danieli Anali Munthu Wachikhulupiriro Cholimba​— Mbali Yoyamba (Danieli 1:1–2:49; 4:1-33)

  • 4:20 ‘Menya Mwamphamvu Nkhondo Yachikhulupiriro’ (Yuda 3; Miyambo 14:15; Aroma 16:17)

  • 4:55 Nyimbo Na. 38 ndi Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena